
Hadith #357
Chichewa (Chicheŵa)Uopeni umbombo chifukwa umbombo unaonongesa mibado yomwe inalipo inu musanabwere, mpakana anaphana komanso anaziloleza zinthu zomwe zinali zoletsedwa kwa iwo.
Reference: صحيح مسلم، كتاب البر والصلة والآداب، باب تحريم الظلم، الحديث 2578