
Hadith #92
Chichewa (Chicheŵa)Silimukhudza Msilamu vuto lina lililonse monga, kutopa, matenda, nkhawa, madandaulo, kupweteka komanso zowawa, ngakhale kubaidwa ndi minga, kupatula kuti (kudzera mu mavutowa) Allah amamuchotsera machimo ake.
Reference: صحيح البخاري، كتاب المرضى، باب ما جاء في كفارة المرض، الحدیث 5641