Hadith #146Hadith #146

Hadith #146

Chichewa (Chicheŵa)

Patsiku la chiweruzo, adzabwera anthu ena mwa asilamu ndi machimo ochuluka ngati mapiri ndipo Allah adzawakhululukira.

Reference: صحيح مسلم، كتاب التوبة، باب قبول توبة القاتل وإن كثر قتله، الحدیث 2767

Available in Other Languages