Hadith #245Hadith #245

Hadith #245

Chichewa (Chicheŵa)

Ndithu manda ndi nyumba yoyamba munyumba za dziko lili nkudza, amene angapulumukemo, umoyo wapambuyo pake udzakhala wosavuta, koma ngati sangapulumuke (m'mandamo), komwe kukubwerako ndikopweteka kwambiri kuposa m'mandamo.

Reference: سنن ابن ماجه، كتاب الزهد، باب ذكر القبر والبلى، الحدیث 4267

Available in Other Languages