
Hadith #297
Chichewa (Chicheŵa)Ndithu Angelo amakhala akumpemphera chikhululuko munthu amene wasala kudya ngati chakudya chitadyedwa (ndi anthu ena) pamaso pake, kufikira anthuwo atamaliza.
Reference: جامع الترمذي، أبواب الصوم، باب ما جاء في فضل الصائم إذا أكل عنده، الحدیث 785