Hadith #202Hadith #202

Hadith #202

Chichewa (Chicheŵa)

Ndili ndi chiyembekezo mwa Allah kuti kusala kwa tsiku la Arafah kumafufuta machimo a chaka cham'mbuyo komanso a chaka chotsatira.

Reference: صحيح مسلم، كتاب الصيام، ‌‌باب استحباب صيام ثلاثة أيام۔۔۔إلخ، الحدیث 1162

Available in Other Languages