Hadith #94Hadith #94

Hadith #94

Chichewa (Chicheŵa)

Munthu wokhulupilira amene amakhala ndi anthu ndikumapilira ku zoipa (zokhumudwitsa) zawo, ndiwabwino kwambiri kuposa munthu amene samakhala limodzi ndi anthu komanso samapilira ku zoipa (zokhumudwitsa) zawo.

Reference: الأدب المفرد للبخاري، باب الذي يصبر على أذى الناس، الحدیث 388

Available in Other Languages