
Hadith #396
Chichewa (Chicheŵa)Munthu amene angaphunzire maphunziro omwe umapeza nawo chisangalalo cha Allah, sakuwaphunzira koma ndi cholinga chopeza za dziko lapansi, sakalimva fungo kaku Janna.
Reference: سنن أبي داود، کتاب العلم، باب في طلب العلم لغير الله تعالى، الحدیث 3664