Hadith #82Hadith #82

Hadith #82

Chichewa (Chicheŵa)

Munthu amene angakonde mzake chifukwa cha Allah, angadane ndi wina wake chifukwa cha Allah, amene amapereka chifukwa cha Allah komanso amaletsa chifukwa cha Allah, ameneyo wakwaniritsa chikhulupiliro chake.

Reference: سنن أبي داود، كتاب السنة، باب الدليل على زيادة الإيمان ونقصانه، الحدیث 4681

Available in Other Languages