
Hadith #160
Chichewa (Chicheŵa)Munthu amene angaiwale kuti wasala ndikudya kapena kumwa, ayenera kupitiriza kusala kwake chifukwa Allah ndi amene wamudyetsa ndikumumwetsa.
Reference: صحيح مسلم، كتاب الصيام، باب أكل الناسي وشربه وجماعه لايفطر، الحدیث 1155