Hadith #236
Chichewa (Chicheŵa)Munthu amene amalimbikira kuthandiza azimayi amene amuna awo anamwalira komanso anthu osauka, ali ngati munthu amene akumenya nkhondo mu njira ya Allah.
Reference: صحيح البخاري، كتاب الأدب، باب الساعي على المسكين، الحدیث 6007