
Hadith #190
Chichewa (Chicheŵa)Munthu akadwala kapena akakhala paulendo, amakhala akulembedwera malipiro ofanana ndi zimene ankachita pamene anali wangwiro komanso asali paulendo.
Reference: صحيح البخاري، كتاب الجهاد والسير، باب يكتب للمسافر مثل ما كان يعمل في الإقامة، الحدیث 2996