Hadith #391Hadith #391

Hadith #391

Chichewa (Chicheŵa)

Mulungu akamfunira zabwino kapolo wake amampatsiratu zilangu pa dziko lapansi pompano, ndipo akamfunira zoipa amamuchedwetsera chilangacho kuti akamulange ndi uchimo wakewo tsiku lomaliza.

Reference: جامع الترمذي، أبواب الزهد، ‌‌باب ما جاء في الصبر على البلاء، الحدیث 2396

Available in Other Languages