Hadith #264Hadith #264

Hadith #264

Chichewa (Chicheŵa)

Mbuye wanga wapamwambamwamba anandilonjeza kuti, anthu okwana zikwi makumi asanu ndi awiri (70,000) azalowa ku mtendere popanda chiwerengero.

Reference: سنن ابن ماجه، ‌‌أبواب الزهد، باب صفة أمة محمد ﷺ، الحدیث 4285

Available in Other Languages