Hadith #313Hadith #313

Hadith #313

Chichewa (Chicheŵa)

Kodi sukudziwa kuti kulowa chisilamu kumafuta machimo akale onse, komanso msamuko umafufuta machimo onse akale monga momwenso mapemphero a Hajji yolandiridwa amafufutira machimo onse akale.

Reference: صحيح مسلم، كتاب الإيمان، باب كون الإسلام يهدم ما قبله وكذا الهجرة والحج، الحدیث 121

Available in Other Languages