
Hadith #349
Chichewa (Chicheŵa)Dziko lapansi ndi lotembeleledwa ndipo chilichonse chili nkati mwakemonso nchotembeleledwa kupatula kumukumbukira Mulungu (dhikri) ndizomwe zimamuwandikisa munthu kwa Mulungu, Munthu ophunzira komanso ndiyemwe akusakasaka ma phunziro adini.
Reference: سنن ابن ماجه، كتاب الزهد، باب مثل الدنيا، الحدیث 4112