Hadith #273Hadith #273

Hadith #273

Chichewa (Chicheŵa)

Chulukitsani kumugwadira Allah, chifukwa ndithu simungamugwadire Allah kamodzi kupatula kuti Allah amakukwezani kudzera mu sajidayo mu ulemelero, komanso amakufufutirani tchimo limodzi.

Reference: صحيح مسلم، كتاب الصلاة، باب فضل السجود والحث عليه، الحدیث 488

Available in Other Languages