
Hadith #1442
Chichewa (Chicheŵa)Chinkati chaka chatsopano kapena mwezi watsopano ukafika, otsatira a Mtumiki Muhammad ﷺ ankaphunzitsana pemphero ili : Kutanthauzira: O Allah! Upangeni (mweziwu/chakachi) kuti tiulowe mwamtendere ndi chikhulupiliro, ndikukhala kwabwino komanso kugonjera, ndichisangalalo chochokera kwa Allah komanso chitetezo kuchokera kwa satana
Reference: المعجم الأوسط للطبراني، باب الميم، من اسمه محمد، الحديث 6241