
Hadith #348
Chichewa (Chicheŵa)Chikhala kuti mwana wa Adam ali ndi chigwa cha Golide akanakondabe atakhala ndi zigwa ziwiri, ndipo palibe chingadzadzitse kamwa yake kupatula dothi ndipo Mulungu amalandira kulapa kwa yemwe walapa.
Reference: صحيح البخاري، كتاب الرقاق، باب ما يتقى من فتنة المال...إلخ، الحدیث 6439