Hadith #377Hadith #377

Hadith #377

Chichewa (Chicheŵa)

Chikhala kuti mumayezamira mwa Allah kuyezamira kwenikweni akanakudyetsani ngati m'mene amadyesera mbalame, zimadzuka kummawa za njala koma zimabwera zitakhuta.

Reference: جامع الترمذي، أبواب الزهد، ‌‌‌باب في التوكل على الله، الحدیث 2344

Available in Other Languages