Hadith #97Hadith #97

Hadith #97

Chichewa (Chicheŵa)

Anthu olungama akupita (akumwalira) m'modzi m'modzi mpakana adzatsala (anthu okhala ngati) madeya monga madeya a tirigu kapena tende. Allah sadzawalabadira mpang'ono pomwe.

Reference: صحيح البخاري، باب ذهاب الصالحين، كتاب الرقاق، الحدیث 6434

Available in Other Languages